Machitidwe a Atumwi 14:18 - Buku Lopatulika18 Pakunena izo, anavutika pakuletsa makamu kuti asapereke nsembe kwa iwo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Pakunena izo, anavutika pakuletsa makamu kuti asapereke nsembe kwa iwo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Ngakhale ndi mau ameneŵa, adavutika kuŵaletsa anthu aja kuti asaŵaphere nsembe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Ngakhale ndi mawu awa, anavutika kuletsa gulu la anthu kuti asapereke nsembe kwa iwo. Onani mutuwo |