Machitidwe a Atumwi 14:14 - Buku Lopatulika14 Pamene anamva atumwi Paulo ndi Barnabasi, anang'amba zofunda zao, natumphira m'khamu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Pamene anamva atumwi Paulo ndi Barnabasi, anang'amba zofunda zao, natumphira m'khamu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Koma pamene atumwi aja, Barnabasi ndi Paulo, adamva zimenezi, adang'amba zovala zao, nathamangira pakati pa anthuwo. Adalankhula mokweza mau kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Koma Barnaba ndi Paulo atamva zimenezi, anangʼamba zovala zawo, nathamangira pakati pa gulu la anthuwo, akufuwula kuti, Onani mutuwo |