Machitidwe a Atumwi 14:10 - Buku Lopatulika10 anati ndi mau aakulu, Taimirira. Ndipo iyeyu anazunzuka, nayenda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 anati ndi mau akulu, Taimirira. Ndipo iyeyu anazunzuka, nayenda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 adanena mokweza mau kuti, “Wongola miyendo yako, imirira.” Pomwepo munthuyo adadzambatuka nkuyamba kuyenda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Ndipo Paulo anamuyitana mofuwula nati, “Imirira!” Atamva zimenezi, munthuyo anayimirira, nayamba kuyenda. Onani mutuwo |