Machitidwe a Atumwi 13:51 - Buku Lopatulika51 Koma iwo, m'mene adawasansira fumbi la ku mapazi ao anadza ku Ikonio. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201451 Koma iwo, m'mene adawasansira fumbi la ku mapazi ao anadza ku Ikonio. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa51 Koma iwo adasansa fumbi la kumapazi kwao moŵatsutsa, napita ku Ikonio. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero51 Tsono iwo anasasa fumbi la ku mapazi awo powatsutsa, ndipo anapita ku Ikoniya. Onani mutuwo |