Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 13:49 - Buku Lopatulika

49 Ndipo mau a Ambuye anabukitsidwa m'dziko lonse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

49 Ndipo mau a Ambuye anabukitsidwa m'dziko lonse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

49 Mau a Ambuye adafalikira m'dziko monse muja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

49 Mawu a Ambuye anafalikira mʼchigawo chonse.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 13:49
8 Mawu Ofanana  

Koma iwo anatulukamo, nabukitsa mbiri yake m'dziko lonselo.


Koma mau a Mulungu anakula, nachulukitsa.


Pamenepo kazembe, pakuona chochitikacho anakhulupirira, nadabwa nacho chiphunzitso cha Ambuye.


Ndipo anachita chomwecho zaka ziwiri; kotero kuti onse akukhala mu Asiya anamva mau a Ambuye, Ayuda ndi Agriki.


Ndipo muona ndi kumva, kuti si pa Efeso pokha, koma monga pa Asiya ponse, Paulo uyu akopa ndi kutembenutsa anthu ambiri, ndi kuti, Si milungu iyi imene ipangidwa ndi manja:


Ndipo mau a Mulungu anakula; ndipo chiwerengero cha ophunzira chidachulukatu ku Yerusalemu; ndipo khamu lalikulu la ansembe linamvera chikhulupirirocho.


Ndipo kudadziwika ku Yopa konse: ndipo ambiri anakhulupirira Ambuye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa