Machitidwe a Atumwi 13:44 - Buku Lopatulika44 Ndipo Sabata linalo udasonkhana pamodzi ngati mzinda wonse kumva mau a Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201444 Ndipo Sabata linalo udasonkhana pamodzi ngati mudzi wonse kumva mau a Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa44 Pa tsiku la Sabata linalo pafupi anthu onse amumzindamo adasonkhana kuti amve mau a Ambuye. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero44 Pa Sabata linalo pafupifupi anthu onse a mu mzindawo anasonkhana kudzamva Mawu a Ambuye. Onani mutuwo |