Machitidwe a Atumwi 13:42 - Buku Lopatulika42 Ndipo pakutuluka iwo anapempha kuti alankhule naonso mau awa Sabata likudzalo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201442 Ndipo pakutuluka iwo anapempha kuti alankhule naonso mau awa Sabata likudzalo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa42 Pamene ankatuluka, anthu aja adapempha Paulo ndi Barnabasi kuti adzaŵakambirenso zomwezi tsiku la Sabata linalo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero42 Pamene Paulo ndi Barnaba amatuluka mʼSunagoge, anthu anawapempha kuti adzapitirize kuyankhula zinthu zimenezi Sabata linalo. Onani mutuwo |