Machitidwe a Atumwi 13:40 - Buku Lopatulika40 Chifukwa chake penyerani, kuti chingadzere inu chonenedwa ndi aneneriwo: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 Chifukwa chake penyerani, kuti chingadzere inu chonenedwa ndi aneneriwo: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 Ndiye inu chenjerani kuti zingakugwereni zimene aneneri aja adanena kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 Samalani kuti zimene aneneri akunena zisakuchitikireni inu: Onani mutuwo |