Machitidwe a Atumwi 13:32 - Buku Lopatulika32 Ndipo ife tikulalikirani inu Uthenga Wabwino wa lonjezano lochitidwa kwa makolo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Ndipo ife tikulalikirani inu Uthenga Wabwino wa lonjezano lochitidwa kwa makolo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Ndipo ife tikukulalikirani Uthenga Wabwino wakuti zilipo zimene Mulungu adaaŵalonjeza makolo athu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 “Ife tikukuwuzani Uthenga Wabwino; umene Mulungu analonjeza makolo athu. Onani mutuwo |