Machitidwe a Atumwi 13:24 - Buku Lopatulika24 Yohane atalalikiratu, asanafike Iye, ubatizo wa kulapa kwa anthu onse a Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Yohane atalalikiratu, asanafike Iye, ubatizo wa kulapa kwa anthu onse a Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Iyeyo asanayambe ntchito, Yohane ankalalikira Aisraele onse kuti atembenuke mtima ndi kubatizidwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Yesu asanabwere, Yohane analalikira kwa anthu onse Aisraeli za kutembenuka mtima ndi ubatizo. Onani mutuwo |