Machitidwe a Atumwi 13:20 - Buku Lopatulika20 ndipo zitatha izi anawapatsa oweruza kufikira Samuele mneneriyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 ndipo zitatha izi anawapatsa oweruza kufikira Samuele mneneriyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 “Pambuyo pake adaŵapatsa oweruza kufikira nthaŵi ya mneneri Samuele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Izi zonse zinatenga zaka 450. “Zitatha izi, Mulungu anawapatsa oweruza mpaka nthawi ya mneneri Samueli. Onani mutuwo |