Machitidwe a Atumwi 13:19 - Buku Lopatulika19 Ndipo m'mene adaononga mitundu ya anthu isanu ndi iwiri mu Kanani, anawapatsa cholowa dziko lao, monga zaka mazana anai kudza makumi asanu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Ndipo m'mene adaononga mitundu ya anthu isanu ndi iwiri m'Kanani, anawapatsa cholowa dziko lao, monga zaka mazana anai kudza makumi asanu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Iye adaononga mitundu isanu ndi iŵiri ya anthu m'dziko la Kanani, napereka dziko lao kwa Aisraele kuti likhale laolao. Zonsezi zidatenga zaka ngati 450. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Mulungu anawagonjetsera mitundu isanu ndi iwiri ya ku Kanaani ndipo anapereka dzikolo kwa Israeli kuti likhale lawo. Onani mutuwo |