Machitidwe a Atumwi 13:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo monga nthawi ya zaka makumi anai anawalekerera m'chipululu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo monga nthawi ya zaka makumi anai anawalekerera m'chipululu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 adaŵasamalabe mopirira m'chipululu zaka makumi anai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Ndipo Iye anapirira khalidwe lawo mʼchipululu kwa zaka makumi anayi. Onani mutuwo |