Machitidwe a Atumwi 13:14 - Buku Lopatulika14 Koma iwowa, atapita pochokera ku Perga anafika ku Antiokeya wa mu Pisidiya; ndipo analowa m'sunagoge tsiku la Sabata, nakhala pansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Koma iwowa, atapita pochokera ku Perga anafika ku Antiokeya wa m'Pisidiya; ndipo analowa m'sunagoge tsiku la Sabata, nakhala pansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Kuchokera ku Perga iwo adapitirira nakafika ku Antiokeya m'dera la Pisidiya. Pa tsiku la Sabata adaloŵa m'nyumba yamapempherero ya Ayuda, nakhala pansi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Kuchokera ku Perga anapita ku Pisidiya wa ku Antiokeya. Pa tsiku la Sabata analowa mʼsunagoge, nakhala pansi. Onani mutuwo |