Machitidwe a Atumwi 12:23 - Buku Lopatulika23 Ndipo pomwepo mngelo wa Ambuye anamkantha, chifukwa sanampatse Mulungu ulemerero; ndipo anadyedwa ndi mphutsi, natsirizika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndipo pomwepo mngelo wa Ambuye anamkantha, chifukwa sanampatsa Mulungu ulemerero; ndipo anadyedwa ndi mphutsi, natsirizika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Pompo mngelo wa Ambuye, adamkantha Herodeyo chifukwa sadapereke ulemu kwa Mulungu. Mphutsi zidamudya ndipo adafa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Nthawi yomweyo mngelo wa Mulungu anamukantha chifukwa sanapereke ulemu kwa Mulungu ndipo anadyedwa ndi mphutsi nafa. Onani mutuwo |