Machitidwe a Atumwi 12:21 - Buku Lopatulika21 Ndipo tsiku lopangira Herode anavala zovala zachifumu, nakhala pa mpando wachifumu, nawafotokozera iwo mau a pabwalo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Ndipo tsiku lopangira Herode anavala zovala zachifumu, nakhala pa mpando wachifumu, nawafotokozera iwo mau a pabwalo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Adapangana tsiku, ndipo pa tsikulo Herode adavala zovala zake zachifumu nkukhala pa mpando wake wachifumu, nayamba kuŵalankhula anthu aja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Pa tsiku limene anasankha Herode, atavala zovala zake zaufumu, anakhala pa mpando wake ndipo anayankhula kwa anthuwo. Onani mutuwo |