Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 12:18 - Buku Lopatulika

18 Koma kutacha, panali phokoso lalikulu mwa asilikali, Petro wamuka kuti.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Koma kutacha, panali phokoso lalikulu mwa asilikali, Petro wamuka kuti.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Kutacha, asilikali aja adasokonezeka kwabasi nati, “Petro wapita kuti?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Pamene kunacha kunali phokoso lalikulu pakati pa asilikali, iwo anafunsa kuti, “Kodi chamuchitikira Petro ndi chiyani?”

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 12:18
5 Mawu Ofanana  

Koma m'mene adawatambasulira dzanja akhale chete, anawafotokozera umo adamtulutsira Ambuye m'ndende. Ndipo anati, Muwauze Yakobo ndi abale izi. Ndipo anatuluka napita kwina.


Ndipo pamene Herode adamfunafuna, wosampeza, anafunsitsa odikira nalamulira aphedwe. Ndipo anatsika ku Yudeya kunka ku Kesareya, nakhalabe kumeneko.


Pamene anautsidwa kutulo mdindoyo, anaona kuti pa makomo a ndende panatseguka, ndipo anasolola lupanga lake, nati adziphe yekha, poyesa kuti am'ndende adathawa.


Nthawi yomweyo kunali phokoso lambiri kunena za Njirayo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa