Machitidwe a Atumwi 12:1 - Buku Lopatulika1 Koma nyengo imeneyo Herode mfumu anathira manja ena a mu Mpingo kuwachitira zoipa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Koma nyengo imeneyo Herode mfumu anathira manja ena a m'Mpingo kuwachitira zoipa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Pafupi ngati nthaŵi imeneyo mfumu Herode adagwira ena a mu Mpingo kuti aŵazunze. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Inali nthawi yomweyi imene mfumu Herode anamanga ena a mu mpingo ndi cholinga chakuti awazunze. Onani mutuwo |