Machitidwe a Atumwi 11:30 - Buku Lopatulika30 ichonso anachita, natumiza kwa akulu mwa dzanja la Barnabasi ndi Saulo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 ichonso anachita, natumiza kwa akulu mwa dzanja la Barnabasi ndi Saulo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Zimenezi adachitadi, ndipo anatuma Barnabasi ndi Saulo kukapereka thandizolo kwa akulu a mpingo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Izi anazichitadi ndipo anatuma Barnaba ndi Saulo kukapereka mphatsozo kwa akulu a mpingo. Onani mutuwo |