Machitidwe a Atumwi 11:29 - Buku Lopatulika29 Ndipo ophunzira, yense monga anakhoza, anatsimikiza mtima kutumiza zothandiza abale akukhala mu Yudeya; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Ndipo ophunzira, yense monga anakhoza, anatsimikiza mtima kutumiza zothandiza abale akukhala m'Yudeya; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Pamenepo Akhristu aja adatsimikiza zotumiza thandizo kwa abale okhala ku Yudeya, ndipo kuti aliyense atumize molingana ndi kupata kwake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Ophunzirawo, aliyense monga mwakupata kwake, anatsimikiza kuthandiza abale okhala ku Yudeya. Onani mutuwo |