Machitidwe a Atumwi 11:27 - Buku Lopatulika27 Koma masiku awa aneneri anatsika ku Yerusalemu kudza ku Antiokeya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Koma masiku awa aneneri anatsika ku Yerusalemu kudza ku Antiokeya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Masiku amenewo kudafika aneneri ena ku Antiokeya ochokera ku Yerusalemu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Masiku amenewo ku Antiokeya kunafika aneneri ena ochokera ku Yerusalemu. Onani mutuwo |