Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 11:25 - Buku Lopatulika

25 Ndipo anatuluka kunka ku Tariso kufunafuna Saulo;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Ndipo anatuluka kunka ku Tariso kufunafuna Saulo;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 Pamenepo Barnabasi adapita ku Tariso kukafuna Saulo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 Kenaka Barnaba anapita ku Tarisisi kukafuna Saulo,

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 11:25
6 Mawu Ofanana  

Koma Paulo anati, Ine ndine munthu Myuda, wa ku Tariso wa mu Silisiya, mfulu ya mzinda womveka; ndipo ndikupemphani mundilole ndilankhule ndi anthu.


Ndipo Yosefe, wotchedwa ndi atumwi Barnabasi (ndilo losandulika mwana wa chisangalalo), Mlevi, fuko lake la ku Kipro,


Ndipo Ambuye anati kwa iye, Tauka, pita ku khwalala lotchedwa Lolunjika, ndipo m'nyumba ya Yudasi ufunse za munthu dzina lake Saulo, wa ku Tariso: pakuti taona, alikupemphera


Koma Barnabasi anamtenga, napita naye kwa atumwi, nawafotokozera umo adaonera Ambuye m'njira, ndi kuti analankhula naye, ndi kuti mu Damasiko adanena molimbika mtima m'dzina la Yesu.


Koma m'mene abale anachidziwa, anapita naye ku Kesareya, namtumiza achokeko kunka ku Tariso.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa