Machitidwe a Atumwi 11:22 - Buku Lopatulika22 Ndipo mbiri yao inamveka m'makutu a Mpingo wakukhala mu Yerusalemu; ndipo anatuma Barnabasi apite kufikira ku Antiokeya; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ndipo mbiri yao inamveka m'makutu a Mpingo wakukhala m'Yerusalemu; ndipo anatuma Barnabasi apite kufikira ku Antiokeya; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Mpingo wa ku Yerusalemu utamva zimene zidachitikazo, udatuma Barnabasi ku Antiokeyako. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Mbiri imeneyi inamveka ku mpingo wa ku Yerusalemu ndipo iwo anatumiza Barnaba ku Antiokeya. Onani mutuwo |