Machitidwe a Atumwi 11:21 - Buku Lopatulika21 Ndipo dzanja la Ambuye linali nao; ndi unyinji wakukhulupirira unatembenukira kwa Ambuye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Ndipo dzanja la Ambuye linali nao; ndi unyinji wakukhulupirira unatembenukira kwa Ambuye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Ambuye ankaŵalimbikitsa, mwakuti anthu ambiri adakhulupirira natembenukira kwa Ambuye. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Mphamvu ya Ambuye inali nawo ndipo anthu ambiri anakhulupirira natembenukira kwa Ambuye. Onani mutuwo |