Machitidwe a Atumwi 11:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo m'mene ndinayamba kulankhula, Mzimu Woyera anawagwera, monga anatero ndi ife poyamba paja. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo m'mene ndinayamba kulankhula, Mzimu Woyera anawagwera, monga anatero ndi ife poyamba paja. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Tsono pamene ndidayamba kulankhula, Mzimu Woyera adaŵatsikira iwowo, monga momwe adaatitsikiranso ife poyamba paja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 “Nditangoyamba kuyankhula, Mzimu Woyera anafika pa iwo monga momwe anafikira pa ife poyamba paja. Onani mutuwo |