Machitidwe a Atumwi 11:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo taonani, pomwepo amuna atatu anaima pa khomo la nyumba m'mene munali ife, anatumidwa kwa ine ochokera ku Kesareya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo taonani, pomwepo amuna atatu anaima pa khomo la nyumba m'mene munali ife, anatumidwa kwa ine ochokera ku Kesareya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Nthaŵi yomweyo kudafika anthu atatu kunyumba kumene ndinkakhala. Adaatumidwa kwa ine kuchokera ku Kesareya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 “Nthawi yomweyo anthu atatu amene anatumidwa kuchokera ku Kaisareya anayima pa nyumba yomwe ndimakhalayo. Onani mutuwo |