Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 11:10 - Buku Lopatulika

10 Ndipo ichi chinachitika katatu; ndipo zinakwezekanso zonse kumwamba.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Ndipo ichi chinachitika katatu; ndipo zinakwezekanso zonse kumwamba.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Zimenezi zidachitika katatu, ndipo zonsezo zinatengedwa kupitanso kumwamba.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Zimenezi zinachitika katatu ndipo kenaka zonse zinatengedwa kupita kumwamba.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 11:10
6 Mawu Ofanana  

Pamenepo Balaki anapsa mtima pa Balamu, naomba m'manja; ndipo Balaki anati kwa Balamu, Ndinakuitana kutemberera adani anga, ndipo unawadalitsa ndithu katatu tsopano.


Yesu anayankha, Moyo wako kodi udzautaya chifukwa cha Ine? Indetu, indetu, ndinena kwa iwe, Asanalire tambala udzandikana Ine katatu.


Ananena naye kachitatu, Simoni mwana wa Yona, kodi undikonda Ine? Petro anamva chisoni kuti anati kwa iye kachitatu, Kodi undikonda Ine? Ndipo anati kwa iye, Ambuye, mudziwa Inu zonse; muzindikira kuti ndikukondani Inu. Yesu ananena naye, Dyetsa nkhosa zanga.


Ndipo taonani, pomwepo amuna atatu anaima pa khomo la nyumba m'mene munali ife, anatumidwa kwa ine ochokera ku Kesareya.


Koma mau anayankha nthawi yachiwiri otuluka m'mwamba, Chimene Mulungu anachiyeretsa, usachiyesera chinthu wamba.


Za ichi ndinapemphera Ambuye katatu kuti chichoke kwa ine.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa