Machitidwe a Atumwi 10:47 - Buku Lopatulika47 Kodi pali munthu akhoza kuletsa madzi, kuti asabatizidwe awa, amene alandira Mzimu Woyera ngatinso ife? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201447 Kodi pali munthu akhoza kuletsa madzi, kuti asabatizidwe awa, amene alandira Mzimu Woyera ngatinso ife? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa47 “Anthu aŵa alandira Mzimu Woyera monga ife. Nanga alipo amene angaŵaletse kubatizidwa ndi madzi?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero47 “Kodi alipo amene angawaletse anthu awa kubatizidwa mʼmadzi? Iwotu alandira Mzimu Woyera monga ifenso.” Onani mutuwo |