Machitidwe a Atumwi 10:43 - Buku Lopatulika43 Ameneyu aneneri onse amchitira umboni, kuti onse akumkhulupirira Iye adzalandira chikhululukiro cha machimo ao, mwa dzina lake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201443 Ameneyu aneneri onse amchitira umboni, kuti onse akumkhulupirira Iye adzalandira chikhululukiro cha machimo ao, mwa dzina lake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa43 Aneneri onse adamchitira umboni, ndi kunena kuti chifukwa cha dzina lake, Mulungu adzakhululukira machimo a munthu aliyense wokhulupirira Iyeyu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero43 Aneneri onse achitira Iye umboni kuti aliyense amene akhulupirira Iye amakhululukidwa machimo chifukwa cha dzina lake.” Onani mutuwo |