Machitidwe a Atumwi 10:36 - Buku Lopatulika36 Mau amene anatumiza kwa ana a Israele, akulalikira Uthenga Wabwino wa mtendere mwa Yesu Khristu (ndiye Ambuye wa onse) Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201436 Mau amene anatumiza kwa ana a Israele, akulalikira Uthenga Wabwino wa mtendere mwa Yesu Khristu (ndiye Ambuye wa onse) Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa36 Mukudziŵa kuti adatumizira Aisraele mau ake naŵauza Uthenga Wabwino wa mtendere kudzera mwa Yesu Khristu, amene ali Ambuye a anthu onse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero36 Uwu ndi uthenga umene Mulungu anatumiza kwa Aisraeli, kulalikira Uthenga Wabwino wamtendere mwa Yesu Khristu amene ndi Ambuye wa onse. Onani mutuwo |