Machitidwe a Atumwi 10:31 - Buku Lopatulika31 nati Kornelio, lamveka pemphero lako, ndi zopereka zachifundo zako zakumbukika pamaso pa Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 nati Kornelio, lamveka pemphero lako, ndi zopereka zachifundo zako zakumbukika pamaso pa Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Adandiwuza kuti, ‘Kornelio, Mulungu wamva pemphero lako, ndipo wakumbukira ntchito zako zachifundo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Ndipo anati, ‘Korneliyo, Mulungu wamva mapemphero ako ndipo wakumbukira mphatso zako kwa osauka. Onani mutuwo |