Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 10:27 - Buku Lopatulika

27 Ndipo pakukamba naye, analowa, napeza ambiri atasonkhana;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

27 Ndipo pakukamba naye, analowa, napeza ambiri atasonkhana;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

27 Ndipo akulankhula naye, adaloŵa napeza anthu ambiri atasonkhana.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

27 Akuyankhula naye, Petro analowa mʼnyumba ndipo anapeza gulu lalikulu la anthu litasonkhana.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 10:27
7 Mawu Ofanana  

Ndipo iwowa anakambirana nkhani za izi zonse zidachitika.


Kodi simunena inu, kuti, Yatsala miyezi inai, ndipo kudza kumweta? Onani ndinena kwa inu, Kwezani maso anu, nimuyang'ane m'minda, kuti mwayera kale kufikira kumweta.


Ndipo m'mawa mwake analowa mu Kesareya. Koma Kornelio analikudikira iwo, atasonkhanitsa abale ake ndi mabwenzi ake enieni.


Pamene anafika nasonkhanitsa Mpingo anabwerezanso zomwe Mulungu anachita nao, kuti anatsegulira amitundu pa khomo la chikhulupiriro.


Pakuti panditsegukira pa khomo lalikulu ndi lochititsa, ndipo oletsana nafe ndi ambiri.


Koma pamene ndinadza ku Troasi kudzalalikira Uthenga Wabwino wa Khristu, ndipo pamene padanditsegukira kwa ine pakhomo, mwa Ambuye,


ndi kutipempherera ifenso pomwepo, kuti Mulungu atitsegulire ife pakhomo pa mau, kuti tilankhule chinsinsi cha Khristu; chimenenso ndikhalira m'ndende,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa