Machitidwe a Atumwi 10:24 - Buku Lopatulika24 Ndipo m'mawa mwake analowa mu Kesareya. Koma Kornelio analikudikira iwo, atasonkhanitsa abale ake ndi mabwenzi ake enieni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Ndipo m'mawa mwake analowa m'Kesareya. Koma Kornelio analikudikira iwo, atasonkhanitsa abale ake ndi mabwenzi ake enieni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 M'maŵa mwake adafika ku Kesareya. Kornelio ankaŵadikira, atasonkhanitsa abale ndi abwenzi ake apamtima. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Tsiku linalo Petro anafika ku Kaisareya. Korneliyo anawadikirira ndipo anali atawasonkhanitsa pamodzi abale ake ndi abwenzi ake a pamtima. Onani mutuwo |