Machitidwe a Atumwi 10:20 - Buku Lopatulika20 Komatu tauka, nutsike, ndipo upite nao, wosakayikakayika; pakuti ndawatuma ndine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Komatu tauka, nutsike, ndipo upite nao, wosakayikakayika; pakuti ndawatuma ndine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Nyamuka, tsika, upite nawo osakayika, pakuti ndaŵatuma ndine.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Dzuka, tsika. Usakayike upite nawo pakuti ndawatuma ndine.” Onani mutuwo |