Machitidwe a Atumwi 1:25 - Buku Lopatulika25 alowe malo a utumiki uwu ndi utumwi, kuchokera komwe Yudasi anapatukira, kuti apite kumalo a iye yekha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 alowe malo a utumiki uwu ndi utumwi, kuchokera komwe Yudasi anapatukira, kuti apite kumalo a iye yekha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 kuti alandire ntchito iyi ya utumwi, m'malo mwa Yudasi uja amene adaisiya ndipo adapita ku malo omuyenera.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 kuti atenge ntchito iyi ya utumwi, imene Yudasi anasiya napita kumalo womuyenera.” Onani mutuwo |