Machitidwe a Atumwi 1:24 - Buku Lopatulika24 Ndipo anapemphera, nati, Inu, Ambuye, wozindikira mitima ya onse, sonyezani mwa awa awiri mmodziyo amene munamsankha, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Ndipo anapemphera, nati, Inu, Ambuye, wozindikira mitima ya onse, sonyezani mwa awa awiri mmodziyo amene munamsankha, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Ndipo adapemphera kuti, “Ambuye, Inu amene mumadziŵa mitima ya anthu onse, tiwonetseni ndi uti mwa aŵiriŵa amene mwamusankha Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Kenaka iwo anapemphera nati, “Ambuye mukudziwa mtima wa aliyense. Tionetseni amene mwamusankha mwa awiri awa Onani mutuwo |