Machitidwe a Atumwi 1:17 - Buku Lopatulika17 Chifukwa anali wowerengedwa mwa ife, ndipo analandira gawo lake la utumiki uwu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Chifukwa anali wowerengedwa mwa ife, ndipo analandira gawo lake la utumiki uwu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Yudasiyo anali mmodzi wa gulu lathu, ndipo adaalandira udindo woti azitumikira pamodzi ndi ife. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Iye anali mmodzi wa gulu lathu ndipo anatumikira pamodzi ndi ife.” Onani mutuwo |