Machitidwe a Atumwi 1:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo m'masiku awa anaimirira Petro pakati pa abale, nati (gulu la anthu losonkhana pamalo pomwe ndilo ngati zana limodzi ndi makumi awiri), Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo m'masiku awa anaimirira Petro pakati pa abale, nati (gulu la anthu losonkhana pamalo pomwe ndilo ngati zana limodzi ndi makumi awiri), Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Tsiku lina, patapita masiku angapo, Petro adaimirira pakati pa abale. (Anthuwo onse pamodzi anali ngati 120.) Iye adati, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Pa nthawi imeneyo Petro anayimirira pakati pa okhulupirira (gulu la anthu pafupifupi 120). Onani mutuwo |