Machitidwe a Atumwi 1:14 - Buku Lopatulika14 Iwo onse analikukangalika m'kupemphera, pamodzi ndi akazi, ndi Maria, amake wa Yesu, ndi abale ake omwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Iwo onse analikukangalika m'kupemphera, pamodzi ndi akazi, ndi Maria, amake wa Yesu, ndi abale ake omwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Onseŵa ankalimbikira kupemphera ndi mtima umodzi, pamodzi ndi akazi ena, ndi Maria amai ake a Yesu, ndiponso abale ake a Yesu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Onsewa ndi mtima umodzi anapitiriza kupemphera pamodzi ndi amayi, ndi Mariya amayi ake a Yesu, ndiponso abale ake a Yesu. Onani mutuwo |