Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 9:37 - Buku Lopatulika

37 Ndipo panali, m'mawa mwake, atatsika m'phiri, khamu lalikulu la anthu linakomana naye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

37 Ndipo panali, m'mawa mwake, atatsika m'phiri, khamu lalikulu la anthu linakomana naye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

37 M'maŵa mwake Yesu ndi ophunzira atatuwo adatsika kuphiri kuja, ndipo anthu ambirimbiri adadzamchingamira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

37 Mmawa mwake, akutsika ku phiri, anthu ambiri anakumana naye.

Onani mutuwo Koperani




Luka 9:37
3 Mawu Ofanana  

Ndipo onani, anafuula munthu wa m'khamulo, nanena, nati, Mphunzitsi, ndikupemphani, yang'anirani mwana wanga; chifukwa ndiye mmodzi yekha wa ine:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa