Luka 8:46 - Buku Lopatulika46 Koma Yesu anati, Wina wandikhudza Ine; pakuti ndazindikira Ine kuti mphamvu yatuluka mwa Ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201446 Koma Yesu anati, Wina wandikhudza Ine; pakuti ndazindikira Ine kuti mphamvu yatuluka mwa Ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa46 Koma Yesu adati, “Iyai, wina wandikhudza ndithu. Ndazindikira kuti mphamvu zina zatuluka mwa Ine.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero46 Koma Yesu anati, “Wina wandikhudza; ndikudziwa chifukwa mphamvu yachoka mwa Ine.” Onani mutuwo |