Luka 8:38 - Buku Lopatulika38 Ndipo munthuyo amene ziwanda zinatuluka mwa iye anampempha Iye akhale ndi Iye; koma anamuuza apite, nanena, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201438 Ndipo munthuyo amene ziwanda zinatuluka mwa iye anampempha Iye akhale ndi Iye; koma anamuuza apite, nanena, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa38 Munthu amene adaamtulutsa mizimu yoipa uja adapempha Yesu kuti apite nao. Koma Yesu adamubweza namuuza kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero38 Munthu amene anatulutsidwa ziwanda uja, anapempha Yesu kuti apite nawo, koma Yesu anamubweza nati, Onani mutuwo |