Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 8:26 - Buku Lopatulika

26 Ndipo iwo anakocheza kudooko ku dziko la Agerasa, ndilo lopenyana ndi Galileya.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

26 Ndipo iwo anakocheza kudooko ku dziko la Agerasa, ndilo lopenyana ndi Galileya.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

26 Iwo adafika ku dziko la Ageregesa, limene lidapenyana ndi Galileya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

26 Iwo anawolokera ku chigawo cha Gerasa chimene chili tsidya lina la nyanja kuchokera ku Galileya.

Onani mutuwo Koperani




Luka 8:26
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Iye anati kwa iwo, Chikhulupiriro chanu chili kuti? Ndipo m'kuchita mantha anazizwa iwo, nanena wina ndi mnzake, Uyu ndani nanga, kuti angolamula mphepo ndi madzi, ndipo zimvera Iye?


Ndipo atatuluka pamtunda Iye, anakomana naye mwamuna wa kumzinda, amene anali nazo ziwanda; ndipo masiku ambiri sanavale chovala, nisanakhala m'nyumba, koma m'manda.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa