Luka 7:46 - Buku Lopatulika46 Sunandidzoza mutu wanga ndi mafuta; koma uyu anadzoza mapazi anga ndi mafuta onunkhira bwino. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201446 Sunandidzoza mutu wanga ndi mafuta; koma uyu anadzoza mapazi anga ndi mafuta onunkhira bwino. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa46 Iwe sudandidzoze kumutu kwanga ndi mafuta, koma iyeyu wadzoza mapazi anga ndi mafuta onunkhira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero46 Iwe sunadzoze mutu wanga mafuta, koma iye wadzoza mapazi anga mafuta onunkhira. Onani mutuwo |