Luka 7:33 - Buku Lopatulika33 Pakuti Yohane Mbatizi wafika wosadya mkate ndi wosamwa vinyo; ndipo munena, Ali ndi chiwanda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201433 Pakuti Yohane Mbatizi wafika wosadya mkate ndi wosamwa vinyo; ndipo munena, Ali ndi chiwanda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa33 “Paja Yohane Mbatizi atabwera, ankasala zakudya ndipo sankamwa vinyo, inu nkumati, ‘Adagwidwa ndi mizimu yoipa.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero33 Pakuti Yohane Mʼbatizi sanabwere kudzadya buledi kapena kumwa vinyo, koma inu mumati, ‘Ali ndi chiwanda.’ Onani mutuwo |