Luka 6:15 - Buku Lopatulika15 ndi Mateyu, ndi Tomasi, ndi Yakobo mwana wa Alifeyo, ndi Simoni wotchedwa Zelote, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 ndi Mateyu, ndi Tomasi, ndi Yakobo mwana wa Alifeyo, ndi Simoni wotchedwa Zelote, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Mateyo ndi Tomasi; Yakobe (mwana wa Alifeyo) ndi Simoni (wa m'chipani chandale cha Azelote;) Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Mateyu, Tomasi, Yakobo mwana wa Alufeyo, Simoni amene amatchedwa Zaleti, Onani mutuwo |