Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 24:48 - Buku Lopatulika

48 Inu ndinu mboni za izi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

48 Inu ndinu mboni za izi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

48 Inuyo ndinu mboni zake za zimenezi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

48 Inu ndinu mboni za zimenezi.

Onani mutuwo Koperani




Luka 24:48
14 Mawu Ofanana  

Ndipo inunso muchita umboni, pakuti muli ndi Ine kuyambira chiyambi.


kuyambira ubatizo wa Yohane, kufikira tsiku lija anatengedwa kunka Kumwamba kutisiya ife, mmodzi wa awa akhale mboni ya kuuka kwake pamodzi ndi ife.


Komatu mudzalandira mphamvu, Mzimu Woyera atadza pa inu: ndipo mudzakhala mboni zanga mu Yerusalemu, ndi mu Yudeya monse, ndi mu Samariya, ndi kufikira malekezero ake a dziko.


Ndipo ife ndife mboni za zonse adazichita m'dziko la Ayuda ndi mu Yerusalemu; amenenso anamupha, nampachika pamtengo.


si kwa anthu onse ai, koma kwa mboni zosankhidwiratu ndi Mulungu, ndiwo ife amene tinadya ndi kumwa naye pamodzi, atauka iye kwa akufa.


ndipo anaonekera masiku ambiri ndi iwo amene anamperekeza Iye pokwera ku Yerusalemu kuchokera ku Galileya, amenewo ndiwo akumchitira umboni tsopano kwa anthu.


Yesu ameneyo, Mulungu anamuukitsa; za ichi tili mboni ife tonse.


Ndipo udzamkhalira Iye mboni kwa anthu onse, za izo udaziona ndi kuzimva.


ndipo munamupha Mkulu wa moyo; amene Mulungu anamuukitsa kwa akufa; za ichi ife tili mboni.


Ndipo atumwi anachita umboni ndi mphamvu yaikulu za kuuka kwa Ambuye Yesu; ndipo panali chisomo chachikulu pa iwo onse.


Ndipo ife ndife mboni za zinthu izi; Mzimu Woyeranso, amene Mulungu anapatsa kwa iwo akumvera Iye.


Akulu tsono mwa inu ndiwadandaulira, ine mkulu mnzanu ndi mboni ya zowawa za Khristu, ndinenso wolawana nao ulemerero udzavumbulutsikawo:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa