Luka 24:46 - Buku Lopatulika46 ndipo anati kwa iwo, Kotero kwalembedwa, kuti Khristu amve zowawa, nauke kwa akufa tsiku lachitatu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201446 ndipo anati kwa iwo, Kotero kwalembedwa, kuti Khristu amve zowawa, nauke kwa akufa tsiku lachitatu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa46 Adaŵauza kuti, “Zimene zidalembedwa ndi izi: zakuti Mpulumutsi wolonjezedwa uja adayenera kumva zoŵaŵa, nkuuka kwa akufa patapita masiku atatu, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero46 Iye anawawuza kuti, “Izi ndi zimene zinalembedwa: Khristu adzazunzika ndipo adzauka kwa akufa tsiku lachitatu. Onani mutuwo |