Luka 24:45 - Buku Lopatulika45 Ndipo anawatsegulira mitima yao, kuti adziwitse malembo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201445 Ndipo anawatsegulira mitima yao, kuti adziwitse malembo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa45 Tsono adaŵathandiza kuti amvetse bwino Malembo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero45 Kenaka anawatsekula maganizo kuti azindikire Malemba. Onani mutuwo |