Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 24:45 - Buku Lopatulika

45 Ndipo anawatsegulira mitima yao, kuti adziwitse malembo;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

45 Ndipo anawatsegulira mitima yao, kuti adziwitse malembo;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

45 Tsono adaŵathandiza kuti amvetse bwino Malembo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

45 Kenaka anawatsekula maganizo kuti azindikire Malemba.

Onani mutuwo Koperani




Luka 24:45
13 Mawu Ofanana  

pamenepo atsegula makutu a anthu, nakomera chizindikiro chilangizo chao;


Munditsegulire maso, kuti ndipenye zodabwitsa za m'chilamulo chanu.


Koma Yehova ananena naye, Anampangira munthu m'kamwa ndani? Kapena analenga munthu wosalankhula ndani, kapena wogontha, kapena wamaso, kapena wakhungu? Si ndine Yehova kodi?


Ndipo anati wina kwa mnzake, Mtima wathu sunali wotentha m'kati mwathu nanga m'mene analankhula nafe m'njira, m'mene anatitsegulira malembo?


Ndipo anatimva mkazi wina dzina lake Lidia, wakugulitsa chibakuwa, wa kumzinda wa Tiatira, amene anapembedza Mulungu; mtima wake Ambuye anatsegula; kuti amvere zimene anazinena Paulo.


kukawatsegulira maso ao, kuti atembenuke kuchokera kumdima, kulinga kukuunika, ndi kuchokera ulamuliro wa Satana kulinga kwa Mulungu, kuti alandire iwo chikhululukiro cha machimo, ndi cholowa mwa iwo akuyeretsedwa ndi chikhulupiriro cha mwa Ine.


Mwa ichi anena, Khala maso wogona iwe, nuuke kwa akufa, ndipo Khristu adzawala pa iwe.


Ndipo tidziwa kuti Mwana wa Mulungu wafika, natipatsa ife chidziwitso, kuti tizindikire Woonayo, ndipo tili mwa Woonayo, mwa Mwana wake Yesu Khristu. Iye ndiye Mulungu woona ndi moyo wosatha.


Ndipo kwa mngelo wa Mpingo wa ku Filadelfiya lemba: Izi anena Iye amene ali Woyera, Iye amene ali Woona, Iye wakukhala nacho chifungulo cha Davide, Iye wotsegula, ndipo palibe wina atseka; Iye wotseka, ndipo palibe wina atsegula:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa