Luka 24:40 - Buku Lopatulika40 Ndipo m'mene ananena ichi, anawaonetsera iwo manja ake ndi mapazi ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 Ndipo m'mene ananena ichi, anawaonetsera iwo manja ake ndi mapazi ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 Atanena zimenezi adaŵaonetsa manja ake ndi mapazi ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 Iye atanena izi anawaonetsa manja ake ndi mapazi ake. Onani mutuwo |